Song of Solomon 8:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma munda wanga wamphesa ndi wangawanga, ndiponso wa ine ndekha. Iwe Solomoni, khala nazo ndalama chikwi chimodzi zija, khala nawonso alimi ako mazana aŵiri aja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munda wanga wamipesa, uli pamaso panga ndiwo wangatu; nacho chikwicho, Solomoni iwe, koma olima zipatso zake azilandira mazana awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma munda wanga wampesa ndi wangawanga ndiponso wa ine ndekha. Iwe Solomoni, khala nazo ndalama zasiliva 1,000 ndipo ndalama zasiliva 200 ndi za amene akusamalira mundawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munda wanga wamipesa, uli pamaso panga ndiwo wangatu; Naco cikwico, Solomo iwe, Koma olima zipatso zace azilandira mazana awiri.