Song of Solomon 8:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Fulumiratu wokondedwa wanga, khala ngati mphoyo kapena ngati mwanawambaŵala wothamanga m'mapiri, m'mene mumamera mbeu zokometsera chakudya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Dzifulumira, mnyamatawe wokondedwa wanga, dzifanane ngati mphoyo pena mwana wa mbawala pa mapiri a mphoka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Fulumira wokondedwa wanga, ndipo ukhale ngati gwape kapena mwana wa mbawala wothamanga mʼmapiri mʼmene mumamera mbewu zokometsera chakudya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Dzifulumira, mnyamatawe wokondedwa wanga, Dzifanane ngati mphoyo pena mwana wa mbawala Pa mapiri a mphoka,