Song of Solomon 8:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikadakutenga nkukuloŵetsa m'nyumba ya amai anga, m'chipinda cha amene adandibala. Ndikadakupatsa vinyo wotsekemera kuti umwe, ndi madzi a makangaza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikadakutsogolera, kukulowetsa m'nyumba ya amai, kuti andilange mwambo; ndikadakumwetsa vinyo wokoleretsa, ndi madzi a makangaza anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndikanakutenga ndi kukulowetsa mʼnyumba ya amayi anga, amayi amene anandiphunzitsa, ndikanakupatsa vinyo wotsekemera kuti umwe, zotsekemera za makangadza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikadakutsogolera, kukulowetsa m'nyumba ya amai, Kuti andilange mwambo; Ndikadakumwetsa vinyo wokoleretsa, Ndi madzi a makangaza anga.