Song of Solomon 8:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, ngakhale madzi a chigumula sangachikokolole. Ngakhale munthu atapereka chuma chonse cha m'nyumba chifukwa chofuna kugula chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu. Alongo a Mkazi
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Madzi ambiri sangazimitse chikondi, ngakhale mitsinje yodzala kuchikokolola: Mwamuna akapereka katundu yense wa m'nyumba yake ngati sintho la chikondi, akanyozedwa ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, mitsinje singachikokolole chikondicho. Ngati wina apereka chuma chonse cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Madzi ambiri sangazimitse cikondi, Ngakhale mitsinje yodzala kucikokolola: Mwamuna akapereka katundu yense wa m'nyumba yace ngati sintho la cikondi, Akanyozedwa ndithu.