Song of Solomon 8:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye akakhala ngati khoma, tidzammangira nsanja yasiliva. Koma akakhala ngati chitseko, tidzamchinga ndi matabwa amkungudza. Mkazi
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati ndiye khoma, tidzamanga pa iye nsanja yasiliva: Ngati ndiye chitseko tidzamtsekereza ndi matabwa amikungudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati iye ndi khoma, tidzamumangira nsanja ya siliva. Ngati iye ndi chitseko, tidzamutchinga ndi matabwa a mkungudza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati ndiye khoma, tidzamanga pa iye nsanja yasiliva: Ngati ndiye citseko tidzamtsekereza ndi matabwa amikungudza.