Titus 2:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Antchito azimvera ambuye ao, aziŵakondweretsa pa zonse. Asamatsutsana nawo
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;