Titus 3:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pamenepo Mulungu Mpulumutsi wathu adaonetsa kukoma kwake ndiponso chifundo chokonda anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pamene kukoma mtima, ndi chikondi cha pa anthu, cha Mpulumutsi wathu Mulungu zidanoneka,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma kukoma mtima ndi chikondi cha Mulungu Mpulumutsi wathu chitaonekera,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pamene kukoma mtima, ndi cikondi ca pa anthu, ca Mpulumutsi wathu Mulungu zidaoneka,