Zechariah 14:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu adzakhala ku Yerusalemu mwamtendere, poti sadzaopsezedwanso ndi chiwonongeko kumeneko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anthu adzakhala m'menemo, ndipo sipadzakhalanso kuonongetsa; koma Yerusalemu adzakhala mosatekeseka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmenemo mudzakhala anthu; sadzawonongedwanso. Yerusalemu adzakhala pa mtendere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anthu adzakhala m'menemo, ndipo sipadzakhalanso kuonongetsa; koma Yerusalemu adzakhala mosatekeseka.