Zechariah 14:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati mabanja ena pa dziko lapansi sadzapita ku Yerusalemu kukapembedza Mfumu, Chauta Wamphamvuzonse, mvula sidzaŵagwera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzachitika kuti aliyense wa mabanja a dziko wosakwera kunka ku Yerusalemu kulambira mfumu Yehova wa makamu, pa iwowa sipadzakhala mvula.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati mitundu ina ya anthu pa dziko lapansi sidzapita ku Yerusalemu kukapembedza Mfumu Yehova Wamphamvuzonse, idzakhala wopanda mvula.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzacitika kuti ali yense wa mabanja a dziko wosakwera kumka ku Yerusalemu kulambira mfumu Yehova wa makamu, pa iwowa sipadzakhala mvula.