Zechariah 2:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu nonsenu, ingokhalani chete pamaso pa Chauta, chifukwa wadzambatuka ndi kutuluka ku malo ake oyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Khalani chete, anthu onse, pamaso pa Yehova; pakuti wagalamuka mokhalira mwake mopatulika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Khalani chete pamaso pa Yehova anthu nonse, chifukwa Iye wavumbuluka kuchoka ku malo ake opatulika.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Khalani cete, anthu onse, pamaso pa Yehova; pakuti wagalamuka mokhalira mwace mopatulika.