Zechariah 2:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akunena kuti, “Tiyeni, tiyeni, thaŵaniko ku dziko lakumpoto. Paja ndidakumwazirani ku mphepo zinai za mlengalenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Haya, haya, thawani kudziko la kumpoto ati Yehova; pakuti ndinakubalalitsani ngati mphepo zinai za kuthambo, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tulukani! Tulukani! Thawaniko ku dziko la kumpoto,” akutero Yehova, “pakuti ndinakumwazirani ku mphepo zinayi zamlengalenga,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Haya, haya, thawani ku dziko la kumpoto, ati Yehova; pakuti ndinakubalalitsani ngati mphepo zinai za kuthambo, ati Yehova.