Zechariah 2:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tiyeni, thaŵirani ku Ziyoni, inu amene mudatengedwa ukapolo kupita ku Babiloni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Haya Ziyoni, thawa iwe wakukhala ndi mwana wamkazi wa Babiloni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tuluka, iwe Ziyoni! Thawa, iwe amene umakhala mʼdziko la mwana wamkazi wa Babuloni!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Haya Ziyoni, thawa iwe wakukhala ndi mwana wamkazi wa Babulo.