Zechariah 7:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma iwowo adakana kumvera, adandifulatira ndi mtima wokanika. Adatseka makutu ao kuti asamve.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma makolo anu anakana kumvera uthenga umenewu; anawumitsa mtima nandifulatira, natseka makutu awo kuti asamve.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve.