Zechariah 9:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dzikolo lidzakhaladi lokongola kwambiri. Tirigu adzalimbitsa anyamata, ndipo vinyo watsopano adzakometsa anamwali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ukoma wake ndi waukulu ndithu, ndi kukongola kwake nkwakukulu ndithu! Tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani chikoka ndi kukongola kwawo! Tirigu adzasangalatsa anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ukoma wace ndi waukuru ndithu, ndi kukongola kwace nkwa kukuru ndithu! tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.