Zechariah 9:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndi wa Chautanso mzinda wa Hamati, umene ukuchitana malire ndi maikowo, chimodzimodzinso Tiro ndi Sidoni ngakhale ndi anzeru kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Hamati yemwe wogundana naye malire; Tiro ndi Sidoni, angakhale ali ndi nzeru zambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli, komanso pa Turo ndi Sidoni, ngakhale kuti iwo ndi anzeru kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Hamati yemwe wogundana naye malire; Turo ndi Zidoni, angakhale ali ndi nzeru zambiri.