Zechariah 9:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ku Asidodi kudzakhala anthu achimsakaniza. Chauta akuti, “Ndidzathetsa kunyada kwa Filistiya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi mtundu wa anthu osokonezeka udzakhala m'Asidodi, ndipo ndidzaononga kudzikuza kwa Afilisti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mu Asidodi mudzakhala mlendo, ndipo ndidzathetsa kunyada kwa Afilisti.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi mtundu wa anthu osokonezeka udzakhala m'Asidodi, ndipo ndidzaononga kudzikuza kwa Afilisti.