Zephaniah 1:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzafafanizanso amene amaŵerama pa madenga ao nkumapembedza dzuŵa, mwezi ndi nyenyezi. Ndidzaononganso amene amati kwinaku akulambira Chauta ndi kulumbira m'dzina lake, kwinaku nkumalumbira m'dzina la Milikomu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
amene amagwada pa madenga a nyumba zawo kupembedza zolengedwa zamumlengalenga, amene amagwada ndi kulumbira mʼdzina la Yehova, komanso mʼdzina la Moleki,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu;