Zephaniah 1:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Khalani chete pamaso pa Ambuye Chauta! Tsikutu la Chauta layandikira. Chauta wakonza kuti anthu ake adzaperekedwe ngati nsembe, ndipo wapatuliratu oitanidwa odzapereka nsembeyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Khala chete pamaso pa Ambuye Yehova; pakuti tsiku la Yehova liyandikira; pakuti Yehova wakonzeratu nsembe, anapatula oitanidwa ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Khalani chete pamaso pa Ambuye Yehova, chifukwa tsiku la Yehova layandikira. Yehova wakonzekera kupereka nsembe; wapatula iwo amene wawayitana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Khala cete pamaso pa Ambuye Yehova; pakuti tsiku la Yehova liyandikira; pakuti Yehova wakonzeratu nsembe, anapatula oitanidwa ace.