Zephaniah 2:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Chauta adzaŵaopsa kwambiri. Adzaononga milungu yonse ya pa dziko lapansi. Mitundu yonse ya anthu idzampembedza Chauta, mtundu uliwonse ku dziko lakwao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova adzawakhalira woopsa; pakuti adzaondetsa milungu yonse ya pa dziko lapansi; ndipo adzamlambira Iye, yense pamalo pake, a m'zisumbu zonse za amitundu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova adzawachititsa mantha kwambiri pamene adzawononga milungu yonse ya mʼdzikomo. Ndipo mitundu ya anthu pa dziko lonse idzamulambira, uliwonse ku dziko la kwawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova adzawakhalira woopsa; pakuti adzaondetsa milungu yonse ya pa dziko lapansi; ndipo adzamlambira Iye, yense pamalo pace, a m'zisumbu zonse za amitundu.