Zephaniah 2:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsoka kwa inu okhala m'mbali mwa nyanja, inu mtundu wa Akeretinu Mau a Chauta akukudzudzulani, inu anthu a ku Kanani, dziko la Afilisti, akuti, “Ndidzakuwonongani nonse sipadzatsala ndi mmodzi yemwe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsoka, okhala m'dziko la kunyanja, mtundu wa Akereti! Mau a Yehova atsutsana nawe, Kanani, dziko la Afilisti; ndidzakuononga, kuti pasakhale wokhala m'dziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsoka inu okhala mʼmbali mwa nyanja, inu mtundu wa Akereti; mawu a Yehova akutsutsa iwe Kanaani, dziko la Afilisti. “Ndidzakuwononga ndipo palibe amene adzatsale.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsoka, okhala m'dziko la kunyanja, mtundu wa Akereti! Mau a Yehova atsutsana nawe, Kanani, dziko la Afilisti; ndidzakuononga, kuti pasakhale wokhala m'dziko.