Zephaniah 3:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Pamenepo ndidzasintha malankhulidwe a mitundu yonse, nkuŵapatsa malankhulidwe abwino, kuti onse azitama dzina la Chauta mopemba ndi kumamtumikira mogwirizana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti pamenepo ndidzapatsa mitundu ya anthu mlomo woyera, kuti onsewa aitanire pa dzina la Yehova kumtumikira ndi mtima umodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pamenepo ndidzayeretsa milomo ya anthu a mitundu yonse kuti anthu onsewo ayitane dzina la Yehova ndi kumutumikira Iye pamodzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti pamenepo ndidzapatsa mitundu ya anthu mlomo woyera, kuti onsewa aitanire pa dzina la Yehova kumtumikira ndi mtima umodzi.