bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
/
1 Chronicles 25
1 Chronicles 25
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
← Chapter 24
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 26 →
1
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. — 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. — 12
10
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. — 12
11
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. — 12
12
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. — 12
13
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. — 12
14
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. — 12
15
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. — 12
16
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. — 12
17
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. — 12
18
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. — 12
19
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. — 12
20
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. — 12
21
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. — 12
22
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. — 12
23
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. — 12
24
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. — 12
25
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. — 12
26
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. — 12
27
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. — 12
28
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. — 12
29
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. — 12
30
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. — 12
31
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake — 12.
← Chapter 24
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 26 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29