Zonsezi zidzatero kuti pasakhale mtengo ndi umodzi womwe wa m'mbali mwa mtsinje umene udzatalike kwambiri, kapena umene nsonga zake zidzafike ku mitambo. Ndiponso pasadzakhale mitengo ina yolandira bwino madzi, imene msinkhu wake ungafike ku mitambo. Pakuti yonseyo kutha kwake ndi kufa, kupita kunsi kwa dziko lapansi, kukakhala pamodzi ndi anthu akufa, amene adaloŵa kale m'manda.
What Does This Mean?
Ezekiel 31:14 says that God will humble all proud trees by the water, showing that no one can be arrogant. God is speaking, warning that pride leads to downfall, and everyone will face death.
Explained for Children
Imagine a forest where tall trees think they're better than the others. God says that even these tall trees will be brought down, just like everyone else. It's like saying no one is too big to be humble.
Historical Background
Ezekiel wrote this around 591 BCE while in exile in Babylon. The message was directed to the people of Israel and the surrounding nations, warning against pride and reminding of God's sovereignty.
Living It Out Today
In today's world, this verse can remind business leaders not to become arrogant with their success. Just like the trees, they too will face challenges and need to stay humble.