bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
/
Job 26
Job 26
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
← Chapter 25
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 27 →
1
Koma Yobu anayankha, nati,
2
Wamthandiza bwanji wopanda mphamvu, Kulipulumutsa dzanja losalimba!
3
Wampangira bwanji wopanda nzeruyu! Ndi kudziwitsa nzeru zeni zeni mocurukal
4
Wafotokozera yani mau? Ndi mzimu wa yani unaturuka mwa iwe?
5
Adafawo anjenjemera Pansi pa madzi ndi zokhalamo,
6
Kumanda kuli padagu pamaso pace, Ndi kucionongeko kusowa cophimbako,
7
Ayala kumpoto popanda kanthu, Nalenjeka dziko pacabe.
8
Amanga madzi m'mitambo yace yocindikira; Ndi mtambo sung'ambika pansi pace,
9
Acingira pa mpando wace wacifumu, Nayalapo mtambo wace.
10
Analembera madziwo malire, Mpaka polekeza kuunika ndi mdima.
11
Mizati ya thambo injenjemera, Ndi kudabwa pa kudzudzula kwace.
12
Mwa mphamvu yace agwetsa nyanja bata; Ndipo mwa luntha lace akantha kudzikuza kwace.
13
Mwa mzimu wace anyezimiritsa thambo; Dzanja lace linapyoza njoka yothawayo.
14
Taonani, awa ndi malekezero a njira zace; Ndi cimene tikumva za Iye ndi cinong'onezo cacing'ono; Koma kugunda kwa mphamvu yace akuzindikiritsa ndani?
← Chapter 25
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 27 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42