bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
1 Chronicles 20
1 Chronicles 20
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 19
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 21 →
1
Itayamba nthaŵi ya phukira chaka chotsatira, nthaŵi imene mafumu ankapita kukamenya nkhondo, Yowabu adatsogolera gulu lankhondo, nakaononga dziko la Aamoni, kenaka adapita kuti akazinge mzinda wa Raba ndi zithando zankhondo. Koma Davide adatsalira ku Yerusalemu. Tsono Yowabu adakantha mzinda wa Raba naugwetsa.
2
Davide adaivula chisoti chagolide mfumu yao, ndipo atachiyesa, adapeza kuti chinkalemera makilogramu 5, ndipo pachisotipo panali mwala wamtengowapatali. Davide adachivala chisoticho, natenga zofunkha zochuluka mumzindamo.
3
Adaŵatulutsa anthu amumzindamo, nakaŵagwiritsa ntchito ndi masowo, zikumbiro zachitsulo ndi nkhwangwa. Umu ndimo m'mene Davide adachitira ndi mizinda yonse ya Aamoni. Pambuyo pake Davideyo adabwerera ku Yerusalemu pamodzi ndi ankhondo onse.
4
Zitapita zimenezi, padauka nkhondo pakati pa Aisraele ndi Afilisti ku Gezere. Tsono Sibekai Muhusati adapha Sipai amene anali mmodzi mwa zidzukulu za ziphona zija zotchedwa Arefaimu, ndipo Afilisti adagonjetsedwa.
5
Kenaka padaukanso nkhondo ndi Afilisti. Tsono Elihanani, mwana wa Yairi, adapha Lami, mbale wa Goliyati Mgiti, amene thunthu la mkondo wake linali lalikulu ngati mtanda woombera nsalu.
6
Panalinso nkhondo ku Gati kumene kunali munthu wina wamtali, wa zala zakumanja uku zisanu ndi chimodzi uku zisanu ndi chimodzi, zakumwendonso uku zisanu nndi chimodzi uku zisanu ndi chimodzi, zonse pamodzi zala 24. Iyeyonso anali mmodzi mwa zidzukulu za Arefaimu.
7
Tsiku lina pamene adanyoza Aisraele, Yonatani, mwana wa Simea, mbale wake wa Davide, adamupha.
8
Anthuwo anali zidzukulu za Arefaimu a ku Gati, ndipo adaphedwa ndi Davide ndi ankhondo ake.
← Chapter 19
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 21 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29