bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
2 Chronicles 19
2 Chronicles 19
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 18
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 20 →
1
Yehosafati mfumu ya ku Yuda adabwerera kunyumba kwake ku Yerusalemu mwamtendere.
2
Koma mneneri Yehu, mwana wa Hanani, adatuluka kuti akumane naye, ndipo adafunsa mfumu Yehosafati kuti, “Kodi ndi bwino kuŵathandiza anthu oipa amene amadana ndi Chauta? Chifukwa cha zimenezi mkwiyo wa Chauta ulikudza kwa inu.
3
Komabe pali zina zabwino zimene mudachita, pakuti mudaononga mafano a m'dziko muno, ndipo mwakhala mukulimbikira ndi mtima wonse kufunafuna Mulungu.”
4
Yehosafati ankakhala ku Yerusalemu. Adayendera anthu kuchokera ku Beereseba mpaka ku dziko lamapiri la ku Efuremu, naŵabweza kwa Chauta, Mulungu wa makolo ao.
5
Adaika anthu oweruza m'dzikomo, mu mzinda uliwonse wamalinga wa ku Yuda.
6
Tsono adauza aweruziwo kuti, “Muganize bwino zimene mukuchita, pakuti simukuweruza m'dzina la munthu ai, koma m'dzina la Chauta. Chautayo ali nanu pamene mukuweruza.
7
Tsono khalani anthu oopa Chauta. Muzisamala zimene mukuchita, pakuti Chauta, Mulungu wathu, sapotoza chiweruzo, kapena kukondera, kapenanso kulandira ziphuphu.”
8
Ku Yerusalemuko Yehosafati adaika Alevi ena ndi ansembe ndiponso akulu a mabanja a Aisraele, kuti aziweruza m'dzina la Chauta ndi kugamula milandu ya anthu. Iwoŵa ankakhala ku Yerusalemu.
9
Adaŵalamula kuti, “Muzichita ntchito imeneyi moopa Chauta, mokhulupirika, ndiponso ndi mtima wonse.
10
Pakakhala mlandu wokhudza abale anu amene akukhala m'mizinda yao, monga mlandu wokhetsa magazi, kapena mlandu wa kusamvera malamulo kapena malangizo kapena zogamula zina, muziŵaphunzitsa nthaŵi zonse kuti asamachimwe pamaso pa Chauta. Motero mkwiyo wa Chauta sudzakugwerani inuyo ndi abale anu. Muzichita choncho, ndipo simudzachimwa konse.
11
Tsono Amariya, mkulu wa ansembe, ndiye adzakhale wokutsogolerani pa zonse zokhudza Chauta. Zebadiya mwana wa Ismaele, kazembe wa fuko la Yuda, ndiye aziyang'anira zonse zokhudza mfumu. Ndipo Alevi adzakutumikirani ngati akapitao. Muzichita zimenezi molimba mtima, Chauta akhale naye amene ali wolungama.”
← Chapter 18
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 20 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36