bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
2 Chronicles 27
2 Chronicles 27
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 26
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 28 →
1
Yotamu anali wa zaka 25 pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 16 ku Yerusalemu. Mai wake anali Yerusa mwana wa Zadoki.
2
Iyeyo adachita zolungama pamaso pa Chauta, kutsata zonse zimene ankachita Uziya, bambo wake, kupatula kuti sadakaloŵe mwamphamvu ku Nyumba ya Chauta. Koma anthu ankachitabe zoipa.
3
Iyeyo adamanga khomo lapamwamba la ku Nyumba ya Chauta, ndipo adagwira ntchito yaikulu yomanga linga la Ofele.
4
Komanso adamanga mizinda ku dziko lonse lamapiri la Yuda. Adamanganso malinga ndi nsanja ku nkhalango zakumapiri.
5
Adamenyana nkhondo ndi mfumu ya Aamoni, ndipo adaŵagonjetsa Aamoniwo. Nchifukwa chake, chaka choyamba Aamoni aja adapereka makilogramu 3,400 a siliva, matani 1,000 a tirigu, ndiponso matani 1,000 a barele. Aamoni ankalipira kwa Yotamuyo zinthu zonga zomwezo pa chaka chachiŵiri ndi chachitatu.
6
Choncho Yotamu adasanduka wamphamvu chifukwa chakuti adasunga makhalidwe oongoka pamaso pa Chauta Mulungu wake.
7
Tsono ntchito zonse za Yotamu, ndi nkhondo zake zonse ndiponso makhalidwe ake, zidalembedwa m'buku la mafumu a ku Israele ndi mafumu a ku Yuda.
8
Iyeyo anali wa zaka 25 pamene ankaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 16 ku Yerusalemu.
9
Pambuyo pake Yotamu adamwalira, naikidwa m'manda mu mzinda wa Davide. Ndipo Ahazi mwana wake adaloŵa ufumu m'malo mwake.
← Chapter 26
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 28 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36