bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Proverbs 5
Proverbs 5
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 4
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 6 →
1
Mwananga, mvera nzeru yanga; tcherera makutu ku luntha langa;
2
ukasunge zolingalira, milomo yako ilabadire zomwe udziwa.
3
Pakuti milomo ya mkazi wachiwerewere ikukha uchi; m'kamwa mwake muti see koposa mafuta.
4
Chimaliziro chake nchowawa ngati chivumulo, ndi chakuthwa ngati lupanga lakuthawa konsekonse.
5
Mayendedwe ake atsikira kuimfa; mapazi ake aumirira kumanda;
6
sasinkhasinkha bwino za njira ya moyo; mayendedwe ake adzandira dzandidzandi osadziwa iye.
7
Ndipo tsopano ana, mundimvere, musapatuke ku mau a m'kamwa mwanga.
8
Siyanitsa njira yako kutali kwa iyeyo, osayandikira ku khomo la nyumba yake;
9
kuti ungapereke ulemu wako kwa ena, ndi zaka zako kwa ankhanza;
10
kuti mphamvu yako isakhutitse alendo, ndi kuti usagwire ntchito m'nyumba ya wachilendo;
11
ungalire pa chimaliziro chako, pothera nyama yako ndi thupi lako;
12
ndi kuti, Bwanji ndinada mwambo, mtima wanga ndi kunyoza chidzudzulo;
13
ndipo sindinamvera mau a aphunzitsi anga; ngakhale kutcherera makutu kwa akundilanga mwambo!
14
Ndikadakhala m'zoipa zonse, m'kati mwa msonkhano ndi khamu la anthu.
15
Imwa madzi a m'chitsime mwako, ndi madzi oyenda a m'kasupe mwako.
16
Kodi magwero ako ayenera kumwazika kunja, ndi mitsinje ya madzi m'makwalala?
17
Ikhale ya iwe wekha, si ya alendo okhala nawe ai.
18
Adalitsike kasupe wako; ukondwere ndi mkazi wokula nayo.
19
Ngati mbawala yokonda ndi chinkhoma chachisomo, maere ake akukwanire nthawi zonse; ukodwe ndi chikondi chake osaleka.
20
Pakuti ukondwerenji, mwananga, ndi mkazi wachiwerewere, ndi kufungatira chifuwa cha mkazi wachilendo?
21
Pakuti njira za munthu zili pamaso pa Yehova, asinkhasinkha za mayendedwe ake onse.
22
Zoipa zakezake zidzagwira woipa; adzamangidwa ndi zingwe za uchimo wake.
23
Adzafa posowa mwambo; adzasochera popusa kwambiri.
← Chapter 4
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 6 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31