bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Proverbs 9
Proverbs 9
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 8
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 10 →
1
Nzeru yamanga nyumba yake, yasema zoimiritsa zake zisanu ndi ziwiri;
2
yaphera nyama yake, nisanganiza vinyo wake, nilongosolanso pa gome lake.
3
Yatuma anamwali ake, iitana pa misanje ya m'mudzi.
4
Wazibwana yense apatukire kuno; iti kwa yense wosowa nzeru,
5
Tiyeni, idyani chakudya changa; nimumwe vinyo wanga ndamsanganiza.
6
Lekani, achibwana inu, nimukhale ndi moyo; nimuyende m'njira ya nzeru.
7
Woweruza munthu wonyoza adzichititsa yekha manyazi; yemwe adzudzula wochimwa angodetsa mbiri yakeyake.
8
Usadzudzule wonyoza kuti angakude; dzudzula wanzeru adzakukonda.
9
Ukachenjeza wanzeru adzakulitsa nzeru yake; ukaphunzitsa wolungama adzaonjezera kuphunzira.
10
Chiyambi cha nzeru ndicho kuopa Yehova; kudziwa Woyerayo ndiko luntha.
11
Pakuti mwa ine masiku ako adzachuluka, zaka za moyo wako zidzaonjezedwa.
12
Ukakhala wanzeru, si yakoyako nzeruyo? Ndipo ukanyoza udzasauka wekha.
13
Utsiru umalongolola, ngwa chibwana osadziwa kanthu.
14
Ukhala pa khomo la nyumba yake, pampando pa misanje ya m'mudzi,
15
kuti uitane akupita panjira, amene angonkabe m'kuyenda kwao,
16
wachibwana ndani? Apatukire kuno. Ati kwa yense wopanda nzeru,
17
madzi akuba atsekemera, ndi chakudya chobisika chikoma.
18
Ndipo mwamunayo sadziwa kuti akufa ali konko; omwe achezetsa utsiru ali m'manda akuya.
← Chapter 8
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 10 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31