bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
Isaiah 50
Isaiah 50
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 49
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 49
Chapter 50
Chapter 51
Chapter 52
Chapter 53
Chapter 54
Chapter 55
Chapter 56
Chapter 57
Chapter 58
Chapter 59
Chapter 60
Chapter 61
Chapter 62
Chapter 63
Chapter 64
Chapter 65
Chapter 66
Chapter 51 →
1
Chauta akuti, “Ili kuti kalata yake imene ndidasudzulira mai wanu? Mwa anthu amene ndili nawo ndi ngongole, ndidakugulitsani kwa uti? Iyai, inutu mudagulitsidwa ku ukapolo chifukwa cha machimo anu, ndipo mai wanu adachotsedwa chifukwa cha upandu wanu.
2
Chifukwa chiyani panalibe anthu, pamene ndidabwera kudzaŵapulumutsa? Chifukwa chiyani panalibe wondiyankha, pamene ndidaitana? Kodi dzanja langa nloti nkulephera kuwombola? Kodi kapena ndilibe mphamvu zopulumutsira? Nditangodzudzula chabe, nyanja yaikulu itha kuuma, ndipo mitsinje itha kusanduka chipululu. Chifukwa chosoŵa madzi nsomba zam'menemo nkuyamba kununkha, ndiponso kufa ndi ludzu.
3
Nditha kuphimba thambo ndi mdima, ndi kulisandutsa ngati likulira maliro.”
4
Ambuye Chauta andiphunzitsa zoyenera kunena, kuti ndidziŵe mau olimbitsa mtima anthu ofooka. M'maŵa mulimonse amandidzutsa, amathwetsa makutu anga kuti ndimve, monga amachitira amene akuphunzira.
5
Ambuye Chauta anditsekula makutu, ndipo sindidaŵanyoze kapena kuŵapandukira.
6
Ndidaperekera msana wanga kwa ondimenya, ndiponso masaya anga kwa ondimwetula ndevu. Sindidaŵabisire nkhope ondinyoza ndi ondithira malovu.
7
Koma kunyoza kwao sindikuvutika nako, chifukwa Ambuye Chauta amandithandiza. Nchifukwa chake ndalimbitsa mtima wanga ngati mwala. Ndikudziŵa kuti sadzandichititsa manyazi.
8
Wondikhalira kumbuyo ali pafupi, ndaninso angandiimbe mlandu? Tipitire limodzi ku bwalo lamilandu. Wofuna kutsutsana nane ndani? Nabwere pafupi.
9
Ambuye Chauta ndi amene amandithandiza, ndani anganene kuti ndine wopalamula? Ndithu, onse ondizenga mlandu adzatheratu. Kutha kwake ngati chovala chodyewa ndi njenjete.
10
Ndani mwa inu amaopa Chauta, ndi kumvera mau a mtumiki wake? Aliyense woyenda mu mdima, wopanda chomuunikira, akhulupirire dzina la Chauta, ndipo adalire Mulungu wake.
11
Nonsenu amene mumasonkha moto ndi kuyatsa zikuni kuti muwononge anzanu, loŵani inuyo m'moto wanu womwewo, yendani pakati pa zikuni zimene mudayatsazo. Mudzakhala m'mazunzo, ndipo ndi Ineyo Chauta amene ndidzagwetsa mazunzowo.
← Chapter 49
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 49
Chapter 50
Chapter 51
Chapter 52
Chapter 53
Chapter 54
Chapter 55
Chapter 56
Chapter 57
Chapter 58
Chapter 59
Chapter 60
Chapter 61
Chapter 62
Chapter 63
Chapter 64
Chapter 65
Chapter 66
Chapter 51 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42
43
44
45
46
47
48
49
50
51
52
53
54
55
56
57
58
59
60
61
62
63
64
65
66