bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 14
Job 14
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 13
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 15 →
1
Munthu wobadwa ndi mkazi ngwa masiku owerengeka, nakhuta mavuto.
2
Atuluka ngati duwa, nafota; athawa ngati mthunzi, osakhalitsa.
3
Ndipo kodi mumtsegulira maso anu wotereyo, ndi kunditenga kunena nane mlandu Inu?
4
Adzatulutsa choyera m'chinthu chodetsa ndani? Nnena mmodzi yense.
5
Popeza masiku ake alembedwa, chiwerengo cha miyezi yake chikhala ndi Inu, ndipo mwamlembera malire ake kuti asapitirirepo iye;
6
mumleke osamthira maso, kuti apumule, kuti akondwere nalo tsiku lake monga wolembedwa ntchito.
7
Pakuti akaulikha mtengo pali chiyembekezo kuti udzaphukanso, ndi kuti nthambi yake yanthete siidzasowa.
8
Ngakhale muzu wake wakalamba m'nthaka, ndi tsinde lake likufa pansi.
9
Koma pa mnunkho wa madzi udzaphuka, nudzaswa nthambi ngati womera.
10
Koma munthu akufa atachita liondeonde inde, munthu apereka mzimu wake, ndipo ali kuti?
11
Madzi achoka m'nyanja, ndi mtsinje ukuphwa, nuuma;
12
momwemo munthu agona pansi, osaukanso; kufikira miyamba kulibe, sadzaukanso, kapena kuutsidwa pa tulo take.
13
Ha? Mukadandibisa kumanda, mukadandisunga m'tseri, mpaka wapita mkwiyo wanu. Mukadandiikira nthawi, ndi kundikumbukira.
14
Atafa munthu, adzakhalanso ndi moyo kodi? Ndikadayembekeza masiku onse a nkhondo yanga, mpaka kwafika kusandulika kwanga.
15
Mukadaitana, ndipo ndikadakuyankhani; mukadakhumba ntchito ya manja anu.
16
Koma tsopano muwerenga moponda mwanga; kodi simuyang'anitsa tchimo langa?
17
Cholakwa changa chaikidwa m'thumba lokhomedwa chizindikiro; ndipo mumanga pamodzi mphulupulu zanga.
18
Ndipo zoonadi, likagwa phiri, latha; ndi thanthwe lisunthika m'malo mwake.
19
Madzi anyenya miyala; zosefukira zao zikokolola fumbi la nthaka; ndipo muononga chiyembekezo cha munthu.
20
Mumlaka chilakire, napita iye; musintha nkhope yake, mumuuza achoke.
21
Ana ake aona ulemu osadziwa iye; napeputsidwa, koma osazindikira za iwo.
22
Koma thupi lake limuwawira yekha, ndi mtima wake umliritsa yekha.
← Chapter 13
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 15 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42