bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 35
Job 35
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 34
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 36 →
1
Ndipo Elihu anabwereza kunena, nati,
2
Kodi muchiyesa choyenera, umo mukuti, Chilungamo changa chiposa cha Mulungu,
3
pakuti munena, Upindulanji nacho? Posachimwa ndinapindula chiyani chimene sindikadapindula pochimwa?
4
Ndidzakuyankhani, ndi anzanu pamodzi ndi inu.
5
Yang'anani kumwamba, nimuone, tapenyani mitambo yokwera yakuposa inu.
6
Ngati mwachimwa, mumchitira Iye chiyani? Zikachuluka zolakwa zanu, mumchitira Iye chiyani?
7
Mukakhala wolungama, mumninkhapo chiyani? Kapena alandira chiyani pa dzanja lanu?
8
Choipa chanu chikhoza kuipira munthu wonga inu, ndi chilungamo chanu chikhoza kukomera wobadwa ndi munthu.
9
Chifukwa cha kuchuluka masautso anthu anafuula, afuula chifukwa cha dzanja la amphamvu.
10
Koma palibe anganene, Ali kuti Mulungu Mlengi wanga, wakupatsa nyimbo usiku;
11
wakutilangiza ife koposa nyama za padziko, wakutipatsa nzeru zoposa mbalame za m'mlengalenga?
12
Apo afuula, koma Iye sawayankha; chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oipa.
13
Zedi Mulungu samvera zachabe, ndi Wamphamvuyonse sazisamalira.
14
Inde mungakhale munena, Sindimpenya, mlanduwo uli pamaso pake, ndipo mumlindira.
15
Ndipo tsopano popeza analibe kumzonda m'kukwiya kwake, ndi kusamalitsa cholakwa,
16
chifukwa chake Yobu anatsegula pakamwa pake mwachabe, nachulukitsa mau opanda nzeru.
← Chapter 34
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 36 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42