bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 7
Job 7
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 6
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 8 →
1
Kodi munthu alibe nkhondo kunja kuno? Kodi masiku ake sakunga masiku a wolembedwa ntchito?
2
Monga kapolo woliralira mthunzi, monga wolembedwa ntchito ayembekezera mphotho yake,
3
momwemo anandilowetsa miyezi yopanda pake. Nandiikiratu zowawa usiku ndi usiku.
4
Ndigona pansi, ndikuti, Ndidzauka liti? Koma usiku undikulira; ndipo ndimapalapata mpaka mbandakucha.
5
Mnofu wanga wavala mphutsi ndi nkanambo zadothi; khungu langa lang'ambika, nilinyansa.
6
Masiku anga afulumira koposa mphindo ya muomba, apitirira opanda chiyembekezo.
7
Kumbukira kuti moyo wanga ndiwo mphepo, diso langa silidzaonanso chokoma.
8
Diso la amene andiona silidzandionanso, maso ako adzandipenyetsetsa, koma ine palibe.
9
Mtambo wapita watha, momwemo wakutsikira kumanda sadzakwerakonso.
10
Sadzabweranso kunyumba yake, osamdziwanso malo ake.
11
Potero sindidzaletsa pakamwa panga; ndidzalankhula popsinjika mu mzimu mwanga; ndidzadandaula pakuwawa mtima wanga.
12
Ndine nyanja kodi, kapena chinjoka cha m'nyanja, kuti Inu mundiikira odikira?
13
Ndikati, Pakama panga mpondisangalatsa, pogona panga padzachepsa chondidandaulitsa;
14
pamenepo mundiopsa ndi maloto, nimundichititsa mantha ndi masomphenya;
15
potero moyo wanga usankha kupotedwa, ndi imfa, koposa mafupa anga awa.
16
Ndinyansidwa nao moyo wanga; sindidzakhala ndi moyo chikhalire; mundileke; pakuti masiku anga ndi achabe.
17
Munthu ndani kuti mumkuze, ndi kuti muike mtima wanu pa iye,
18
ndi kuti mucheze naye m'mawa ndi m'mawa, ndi kumuyesa nthawi zonse?
19
Mukana kundichokera kufikira liti, kapena kundileka mpaka nditameza dovu?
20
Ngati ndachimwa, ndingachitire Inu chiyani, Inu wodikira anthu? Mwandiikiranji ndikhale chandamali chanu? Kuti ndikhale kwa ine ndekha katundu?
21
Mulekeranji kukhululukira kulakwa kwanga ndi kundichotsera mphulupulu yanga? Popeza tsopano ndidzagona kufumbi; mudzandifunafuna, koma ine palibe.
← Chapter 6
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 8 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42