bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 4
Job 4
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 3
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 5 →
1
Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,
2
Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao chisoni? Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?
3
Taona iwe walangiza aunyinji, walimbitsa manja a ofooka.
4
Mau ako anachirikiza iye amene akadagwa, walimbitsanso maondo otewa.
5
Koma tsopano chakufikira iwe, ndipo ukomoka; chikukhudza, ndipo uvutika.
6
Kodi kulimbika mtima kwako si ndiko kuti uopa Mulungu, ndi chiyembekezo chako si ndiwo ungwiro wa njira zako?
7
Takumbukira tsopano, watayika ndani wosapalamula konse? Kapena oongoka mtima alikhidwa kuti?
8
Monga umo, ndaonera, olimira mphulupulu, nabzala vuto, akololapo zomwezo.
9
Atayika ndi mpweya wa Mulungu, nathedwa ndi mpumo wa mkwiyo wake.
10
Kubangula kwa mkango, ndi kulira kwa mkango waukali kwaletsedwa, ndi mano a misona ya mkango athyoledwa.
11
Mkango wokalamba udzifera posowa mkoka, ndi misona ya mkango waukazi imwazika.
12
Anditengera mau m'tseri, m'khutu mwanga ndinalandira kunong'oneza kwake.
13
M'malingaliro a masomphenya a usiku, powagwira anthu tulo tatikulu
14
Anandidzera mantha ndi kunjenjemera, nanthunthumira nako mafupa anga onse.
15
Pamenepo panapita mzimu pamaso panga; tsitsi la thupi langa lidati nyaunyau.
16
Unaima chilili, koma sindinatha kuzindikira maonekedwe ake; panali mzukwa pamaso panga; kunali chete, ndipo ndidamva mau akuti,
17
Kodi munthu adzakhala wolungama ndi kuposa Mulungu? Kodi munthu adzakhala woyera woposa Mlengi wake?
18
Taona, sakhulupirira atumiki ake; nawanenera amithenga ake zopusa;
19
kopambana kotani nanga iwo akukhala m'nyumba zadothi, amene kuzika kwao kuli m'fumbi, angothudzulidwa ngati njenjete.
20
Kuyambira m'mawa kufikira madzulo athudzuka; aonongeka kosatha, osasamalirako munthu.
21
Kukometsetsa kwao sikumachotsedwa nao? Amafa koma opanda nzeru.
← Chapter 3
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 5 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42