bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 23
Job 23
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 22
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 24 →
1
Koma Yobu anayankha, nati,
2
Lero lomwe kudandaula kwanga kumawawa; kulanga kwanga kuposa kubuula kwanga m'kulemera kwake.
3
Ha! Ndikadadziwa kumene ndikampeza Mulungu, kuti ndifike kumpando wake!
4
Ndikadalongosola mlandu wanga pamaso pake, ndikadadzaza m'kamwa mwanga ndi matsutsano.
5
Ndikadadziwa mau akadandiyankha ine, ndikadazindikira chimene akadanena nane.
6
Akadatsutsana nane kodi mwa mphamvu yake yaikulu? Iai, koma akadanditcherera khutu.
7
Apo woongoka mtima akadatsutsana naye; ndipo ndikadapulumuka chipulumukire kwa Woweruza wanga.
8
Taonani, ndikamka m'tsogolo, kulibe Iye; kapena m'mbuyo sindimzindikira;
9
akachita Iye kulamanzere, sindimpenyerera; akabisala kulamanja, sindimuona.
10
Koma adziwa njira ndilowayi; atandiyesa ndidzatuluka ngati golide.
11
Phazi langa lagwiratu moponda Iye, ndasunga njira yake, wosapatukamo.
12
Sindinabwerera kusiya malamulo a pa milomo yake; ndasungitsa mau a pakamwa pake koposa lamulo langalanga.
13
Koma Iye ndiye wa mtima umodzi, adzambweza ndani? Ndi ichi chimene moyo wake uchifuna achichita.
14
Pakuti adzachita chondiikidwiratu; ndipo zambiri zotere zili ndi Iye.
15
Chifukwa chake ndiopsedwa pankhope pake; ndikalingirira, ndichita mantha ndi Iye.
16
Pakuti Mulungu walefula mtima wanga, ndi Wamphamvuyonse wandiopsa.
17
Popeza sindinalikhidwa usanafike mdimawo, ndipo sanandiphimbire nkhope yanga ndi mdima wa bii.
← Chapter 22
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 24 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42