bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 37
Job 37
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 36
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 38 →
1
Pa ichinso mtima wanga unjenjemera, nusunthika m'malo mwake.
2
Mvetsetsani chibumo cha mau ake, ndi kugunda kotuluka m'kamwa mwake.
3
Akumveketsa pansi pa thambo ponse, nang'anipitsa mphezi yake ku malekezero a dziko lapansi.
4
Mau abuma kuitsata, agunda ndi mau a ukulu wake, ndipo sailetsa atamveka mau ake.
5
Mulungu agunda modabwitsa ndi mau ake, achita zazikulu osazidziwa ife.
6
Pakuti anena kwa chipale chofewa, Ugwe padziko, momwemonso kwa mvula, ndi kwa mvumbi waukulu.
7
Atsekereza mokhomera chizindikiro dzanja la munthu aliyense, kuti anthu onse anawalenga adziwe.
8
Pamenepo zilombo zilowa mobisalamo, nizikhala m'ngaka mwao.
9
M'chipinda mwake mutuluka kamvulumvulu, ndi chisanu chifuma kumpoto.
10
Mwa kupuma kwake Mulungu apereka chipale, ndi madzi achitando aundana.
11
Asenzetsanso mtambo wakuda bii madzi, afunyulula mtambo wokhalamo mphezi yake;
12
ndipo utembenukatembenuka pakulangiza kwake, kuti uchite zilizonse aulamulira, pa nkhope ya dziko lokhalamo anthu;
13
ngati aufikitsira dziko lake kulidzudzula, kapena kulichitira chifundo.
14
Tamverani ichi, Yobu. Taimani, mulingirire zodabwitsa za Mulungu.
15
Kodi mudziwa umo Mulungu azilangizira zimenezi, nawalitsa mphezi ya m'mtambo mwake?
16
Kodi mudziwa madendekeredwe ake a mitambo, zodabwitsa za Iye wakudziwa mwangwiro?
17
Kodi mudziwa umo zovala zanu zifundira, pamene dziko lili thuu chifukwa cha mwera?
18
Kodi muyala thambo pamodzi ndi Iye, ndilo lolimba ngati kalirole woyengeka?
19
Mutilangize chimene tidzanena ndi Iye; sitidziwa kulongosola mau athu chifukwa cha mdima.
20
Kodi munthu ayenera kumuuza kuti ndifuna kunena, kapena kodi munthu adzakhumba kumezedwa?
21
Ndipo tsopano anthu sakhoza kupenyerera kuunika pakunyezimira kuthambo, ndi mphepo yapita ndi kuuyeretsa.
22
Kuchokera kumpoto kudzera kuwala konyezimira, Mulungu ali nao ukulu woopsa.
23
Kunena za Wamphamvuyonse, sitingamsanthule; ndiye wa mphamvu yoposa; koma mwa chiweruzo ndi chilungamo chochuluka samasautsa.
24
M'mwemo anthu amuopa, Iye sasamalira aliyense wanzeru mumtima.
← Chapter 36
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 38 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42