bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 18
Job 18
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 17
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 19 →
1
Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha, nati,
2
Musaka mau kufikira liti? Zindikirani, ndi pamenepo tidzanena.
3
Tiyesedwa bwanji ngati nyama za kuthengo, ndi kukhala odetsedwa pamaso panu?
4
Iwe wodzing'amba mumkwiyo mwako, kodi dziko lapansi lisiyidwe chifukwa cha iwe? Kapena thanthwe lisunthike m'malo mwake?
5
Inde, kuunika kwa woipa kudzazima, ndi lawi la moto wake silidzawala.
6
Kuunikaku kudzada m'hema mwake, ndi nyali yake ya pamwamba pake idzazima.
7
Mapondedwe ake amphamvu adzasautsidwa, ndi uphungu wakewake udzamgwetsa.
8
Pakuti aponyedwa m'ukonde ndi mapazi ake, namaponda pamatanda.
9
Msampha udzamgwira kuchitende, ndi khwekhwe lidzamkola.
10
Msampha woponda umbisikira pansi, ndi msampha wa chipeto panjira.
11
Zoopetsa zidzamchititsa mantha monsemo, nadzampirikitsa kumbuyo kwake.
12
Njala idzatha mphamvu yake, ndi tsoka lidzamkonzekeratu pambali pake.
13
Zidzatha ziwalo za thupi lake, mwana woyamba wa imfa adzatha ziwalo zake.
14
Adzazulidwa kuhema kwake kumene anakhulupirira; nadzatengedwa kunka naye kwa mfumu ya zoopsa.
15
Adzakhala m'hema mwake iwo amene sali ake; miyala ya sulufure idzawazika pokhala pake.
16
Mizu yake idzauma pansi, ndi nthambi yake idzafota m'mwamba.
17
Chikumbukiro chake chidzatayika m'dziko, ndipo adzasowa dzina kukhwalala.
18
Adzamkankha achoke kukuunika alowe kumdima; adzampirikitsa achoke m'dziko lokhalamo anthu.
19
Sadzakhala naye mwana kapena chidzukulu mwa anthu a mtundu wake, kapena wina wotsalira kumene anakhalako.
20
Akudza m'mbuyo adzadabwa nalo tsiku lake, monga aja omtsogolera anagwidwa mantha.
21
Zoonadi, zokhalamo osalungama zitero, ndi malo a iye amene sadziwa Mulungu ndi awa.
← Chapter 17
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 19 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42