bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 8
Job 8
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 7
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 9 →
1
Pamenepo anayankha Bilidadi Msuki, nati,
2
Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti?
3
Ngati Mulungu akhotetsa chiweruzo? Ngati Wamphamvuyonse akhotetsa mlandu?
4
Chinkana ana ako anamchimwira Iye, ndipo anawapereka mwa kulakwa kwao;
5
koma ukafunitsitsa Mulungu, ndi kupembedza Wamphamvuyonse;
6
ukakhala woyera ndi woongoka mtima, zoonadi adzakugalamukira tsopano, ndi kupindulitsa pokhala pako polungama.
7
Ndipo chinkana chiyambi chako chinali chaching'ono, chitsiriziro chako chidzachuluka kwambiri.
8
Pakuti ufunsire tsono mbadwo wapitawo, nusamalire zimene makolo ao adazisanthula.
9
Pakuti ife ndife adzulo, osadziwa kanthu, popeza masiku athu a pa dziko lapansi ndiwo ngati mthunzi;
10
amene aja sangakuphunzitse, ndi kukufotokozera, ndi kutulutsa mau a mumtima mwao?
11
Ngati gumbwa aphuka popanda chinyontho? Ngati manchedza amera popanda madzi?
12
Akali auwisi, sanawacheke, auma, asanaume mathengo onse ena.
13
Momwemo mayendedwe a onse oiwala Mulungu; ndi chiyembekezo cha onyoza Mulungu; chidzatayika.
14
Kulimbika mtima kwake kudzathyoka, chikhulupiriro chake chikunga nyumba ya kangaude.
15
Adzatsamira nyumba yake, koma yosamlimbira; adzaiumirira koma yosakhalitsa.
16
Akhala wamuwisi pali dzuwa, ndi nthambi zake zitulukira pamunda pake.
17
Mizu yake iyangayanga pa kasupe wamadzi, apenyerera pokhalapo miyala.
18
Akamuononga kumchotsa pamalo pake, padzamkana, ndi kuti, Sindinakuona.
19
Taona, ichi ndicho chomkondweretsa panjira pake, ndi panthaka padzamera ena.
20
Taona, Mulungu sakana munthu wangwiro; kapena kugwiriziza ochita zoipa.
21
Koma adzadzaza m'kamwa mwako ndi kuseka, ndi milomo yako kufuula.
22
Iwo akudana nawe adzavala manyazi; ndi hema wa oipa adzakhala kuli zii.
← Chapter 7
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 9 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42