bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
/
Job 27
Job 27
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
← Chapter 26
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 28 →
1
Ndipo Yobu anaonjezanso mwambi wake, nati,
2
Pali Mulungu, amene anandichotsera zoyenera ine, ndi Wamphamvuyonse, amene anawawitsa moyo wanga,
3
pakuti moyo wanga wonse ukali mwa ine, ndi mpweya wa Mulungu m'mphuno mwanga;
4
milomo yanga siilankhula chosalungama, ndi lilime langa silitchula zachinyengo.
5
Sindivomereza konse kuti muli olungama; mpaka kufa ine sinditaya ungwiro wanga.
6
Ndiumirira chilungamo changa, osachileka; chikhalire moyo ine, mtima wanga sunditonza.
7
Mdani wanga akhale ngati woipa, ndi iye amene andiukira ngati wosalungama.
8
Pakuti chiyembekezo cha wonyoza Mulungu nchiyani pomlikhatu Mulungu, pomchotsera moyo wake?
9
Kodi Mulungu adzamvera kufuula kwake, ikamdzera nsautso?
10
Kodi adzadzikondweretsa naye Wamphamvuyonse, ndi kuitana kwa Mulungu nthawi zonse?
11
Ndidzakulangizani za dzanja la Mulungu; chokhala ndi Wamphamvuyonse sindidzachibisa.
12
Taonani, inu nonse munachiona; ndipo mugwidwa nazo zopanda pake chifukwa ninji?
13
Ili ndi gawo la munthu woipa kwa Mulungu, ndi cholowa cha akupsinja anzao achilandira kwa Wamphamvuyonse.
14
Akachuluka ana ake, ndiko kuchulukira lupanga, ndi ana ake sadzakhuta chakudya.
15
Akumtsalira iye adzaikidwa muimfa, ndi akazi ake amasiye sadzalira maliro.
16
Chinkana akundika ndalama ngati fumbi, ndi kukonzeratu zovala ngati dothi;
17
azikonzeretu, koma wolungama adzazivala, ndi wosalakwa adzagawa ndalamazo.
18
Amanga nyumba yake ngati kangaude, ndi ngati wolindira amanga dindiro.
19
Agona pansi ali wachuma, koma saikidwa; potsegula maso ake, wafa chikomo.
20
Zoopsa zimgwera ngati madzi; nkhuntho umtenga usiku.
21
Mphepo ya kum'mawa imtenga, nachoka iye; nimkankha achoke m'malo mwake.
22
Pakuti Mulungu adzamponyera zoopsa, osamleka; kuthawa akadathawa m'dzanja lake.
23
Anthu adzamuombera manja, nadzamuimbira mluzu achoke m'malo mwake.
← Chapter 26
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 28 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42