bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
Ezekiel 15
Ezekiel 15
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 14
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 16 →
1
Chauta adandipatsira uthenga uwu wakuti,
2
“Iwe mwana wa munthu, kodi mtengo wamphesa umapambana bwanji wina uliwonse? Nthambi zake zimapambana bwanji nthambi za mitengo ina yakunkhalango?
3
Kodi mtengo umene uja nkupangira chiyani? Kodi anthu angathe kupangira chokolekapo zinthu zao?
4
Ha! Paja ndi nkhuni zosonkhera moto. Tsono moto utapsereza nsonga zake za mtengowo pamodzi ndi mphindikati yake, kodi nkugwira nawonso ntchito ina iliyonse?
5
Ngakhale usanapse, sikukadatheka kugwira nawo ntchito. Nanga nanji utapserera ndi moto, adzaugwiritsa ntchito bwanji?
6
“Nchifukwa chake zimene ndikunena Ine Ambuye Chauta ndi izi: Mtengo wamphesa ndidzauponya m'moto monga momwe ndimachitira mitengo ina yakunkhalango. Momwemonso ndi m'mene ndidzaŵachitire anthu a ku Yerusalemu,
7
ndidzaŵalanga. Ngakhale athaŵe moto, motowo udzaŵatenthabe. Motero mudzadziŵa kuti Ine ndine Chauta, ndikadzaŵalanga.
8
Ndipo dziko laolo ndidzalisandutsa chipululu, chifukwa chakuti iwowo sadakhulupirike. Ndikutero Ine Ambuye Chauta.”
← Chapter 14
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 16 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42
43
44
45
46
47
48