bible
ra
🌐 Language
English
Español
Français
Deutsch
Português
Italiano
Nederlands
Русский
中文
日本語
한국어
العربية
Türkçe
Tiếng Việt
ไทย
Indonesia
All Languages
Home
/
Chewa
/
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
/
Jeremiah 21
Jeremiah 21
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
← Chapter 20
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 49
Chapter 50
Chapter 51
Chapter 52
Chapter 22 →
1
Zedekiya, mfumu ya ku Yuda, adatuma Pasuri mwana wa Malakiya, ndiponso wansembe Zefaniya mwana wa Maseiya, naŵauza kuti,
2
“Pitani kwa Yeremiya mukampemphe kuti atinenere kwa Chauta, popeza kuti Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni akufuna kutithira nkhondo. Mwina mwake Chauta nkutichitira zodabwitsa, kuti Nebukadinezara achoke kwathu kuno.”
3
Koma otumidwa aja atafika, Yeremiya adaŵauza kuti,
4
“Mukamuuze Zedekiya kuti Chauta, Mulungu wa Israele akuti, ‘Ndidzakulandani zida zankhondo zimene zili m'manja mwanuzo, zimene mukumenya nazo nkhondo ndi mfumu ya ku Babiloni ndi ankhondo ake amene akuzingani ndi zithando zankhondo. Ndidzabwera nazo ndi kuziika m'kati mwa mzinda uno.
5
Ineyo mwiniwakene ndi mkono wanga wamphamvu, ndidzamenyana nanu nkhondo inuyo, ndili wopsa mtima, wokalipa ndi wokwiya.
6
Ndidzakantha okhala mumzindamu ndi ziŵeto zomwe, ndipo zonse zidzafa ndi mliri woopsa.
7
Pambuyo pake ndidzapititsa ku ukapolo Zedekiya mfumu ya ku Yuda pamodzi ndi nduna zake, ndi anthu otsala mumzindamu opulumuka ku mliri, ku njala ndi ku nkhondo. Ndidzaŵapereka kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, ndiponso kwa adani ao amene akufuna kuŵapha. Adzaŵaphadi ndi lupanga, sadzaŵamvera chisoni kapena chifundo.’ ”
8
Chauta akunena kuti, “Anthu ameneŵa udzaŵauzenso kuti asankhulepo: kodi afuna moyo kapena imfa?
9
Aliyense wotsala mu mzinda uno adzafa ndi nkhondo, njala kapena mliri. Koma aliyense amene adzadzipereka kwa Ababiloni amene akuzingani ndi zithando zankhondo aja, ameneyo adzakhala ndi moyo, adzapulumuka.
10
Mzinda umenewu ndatsimikiza kuti ndidzauchita zoipa osati zabwino ai. Udzaperekedwa kwa mfumu ya ku Babiloni ndipo iyeyo adzautentha ndi moto.”
11
“Tsono banja laufumu la ku Yuda uliwuze kuti, ‘Imvani mau a Chauta.
12
Inu a m'banja la Davide, Chauta akunena kuti: “ ‘Muziweruza motsata chilungamo m'maŵa mulimonse, ndipo muzipulumutsa kwa anthu ozunza, aliyense amene katundu wake wabedwa, kuwopa kuti mkwiyo wanga ungayake nkukhala wosazimika, chifukwa cha machimo anu.
13
“ ‘Ndikukuimbani mlandu, inu anthu okhala m'chigwa inu okhala ngati thanthwe lapachidikha,’ ” akutero Chauta. “Inu amene mumati, ‘Ndani angatithire nkhondo? Ndani angathe kuloŵa m'malinga mwathu?’
14
Ndidzakulangani potsata ntchito zanu. Ndidzatentha nkhalango yanu, moto udzapsereza zonse zimene zakuzungulirani,” akuterotu Chauta.
← Chapter 20
Jump to:
Chapter 1
Chapter 2
Chapter 3
Chapter 4
Chapter 5
Chapter 6
Chapter 7
Chapter 8
Chapter 9
Chapter 10
Chapter 11
Chapter 12
Chapter 13
Chapter 14
Chapter 15
Chapter 16
Chapter 17
Chapter 18
Chapter 19
Chapter 20
Chapter 21
Chapter 22
Chapter 23
Chapter 24
Chapter 25
Chapter 26
Chapter 27
Chapter 28
Chapter 29
Chapter 30
Chapter 31
Chapter 32
Chapter 33
Chapter 34
Chapter 35
Chapter 36
Chapter 37
Chapter 38
Chapter 39
Chapter 40
Chapter 41
Chapter 42
Chapter 43
Chapter 44
Chapter 45
Chapter 46
Chapter 47
Chapter 48
Chapter 49
Chapter 50
Chapter 51
Chapter 52
Chapter 22 →
All chapters:
1
2
3
4
5
6
7
8
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
19
20
21
22
23
24
25
26
27
28
29
30
31
32
33
34
35
36
37
38
39
40
41
42
43
44
45
46
47
48
49
50
51
52